Chautah

3 views

Lyrics

Chauta woo!
 Tsiku loyamba lomwelija
 Lomwelija
 Limene munali kulenga ine
 Ndilomwelo
 Ndilomweli ndikuti beta munanchinja nkhope
 Chauta woo!
 Tsiku loyamba lomwelija
 Lomwelija
 Limene munali kulenga ine
 Ndilomwelo
 Ndilomweli ndikuti beta munanchinja nkhope
 Nkhope yanga
 Ndikhala ngati ndiliulira
 Nkhope yanga
 Ndikhala ngati ndiliupita or bwera,
 Silidziwika bwino, i
 Koma munakanchinja nkhope
 Nkhope yanga
 Ndikhala ngati ndiliulira
 Nkhope yanga
 Ndikhala ngati ndiliupita or bwera,
 Silidziwika bwino, i
 Koma munakanchinja nkhope
 Oyang'ana (andiyesa Chitsilu yawa)
 Oyang'ana (andiyesa wakuba ine)
 Oyang'ana (andiyesa wolodza)
 Chauta munakanchinja nkhope
 Oyang'ana (andiyesa Chitsilu yawa)
 Oyang'ana (andiyesa wakuba ine)
 Oyang'ana (andiyesa wolodza)
 Chauta ndaona bvuto

Audio Features

Song Details

Duration
07:13
Key
4
Tempo
131 BPM

Share

More Songs by Simon Chimbetu

Similar Songs